Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 17:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Mwana aliyense wamwamuna amene wakwanitsa masiku 8 azidulidwa+ mʼmibadwo yanu yonse. Aliyense amene wabadwira mʼnyumba yanu komanso aliyense amene si mbadwa yanu koma munamugula ndi ndalama kwa mlendo azidulidwa.

  • Genesis 21:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Isaki atakwanitsa masiku 8, Abulahamu anachita mdulidwe wa mwana wakeyo, monga mmene Mulungu anamulamulira.+

  • Luka 1:59
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 59 Pa tsiku la 8, iwo anabwera kudzachita mdulidwe wa mwanayo+ komanso ankafuna kumupatsa dzina la bambo ake, lakuti Zekariya.

  • Luka 2:21, 22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Patatha masiku 8, nthawi yoti achite mdulidwe wa mwanayo itakwana,+ anamupatsa dzina lakuti Yesu. Limeneli ndi dzina limene mngelo uja anatchula Mariya asanakhale woyembekezera.+

      22 Komanso nthawi yoti iwo ayeretsedwe mogwirizana ndi Chilamulo cha Mose itakwana,+ anapita ndi mwanayo ku Yerusalemu kukamupereka kwa Yehova.*

  • Yohane 7:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Pa chifukwa chimenechi Mose anakupatsani mdulidwe.+ Sikuti mdulidwewo ndi wochokera kwa Mose ayi, koma ndi wochokera kwa makolo akale,+ ndipo mumachita mdulidwe tsiku la sabata.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena