Numeri 2:18 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 18 Amene azimanga msasa wawo kumadzulo ndi gulu la mafuko atatu la Efuraimu ndi magulu awo.* Mtsogoleri wa ana a Efuraimu ndi Elisama,+ mwana wa Amihudi. Numeri 10:22 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 22 Ndiyeno gulu la mafuko atatu la ana a Efuraimu linanyamuka potengera magulu awo.* Mtsogoleri wa gululi anali Elisama,+ mwana wa Amihudi.
18 Amene azimanga msasa wawo kumadzulo ndi gulu la mafuko atatu la Efuraimu ndi magulu awo.* Mtsogoleri wa ana a Efuraimu ndi Elisama,+ mwana wa Amihudi.
22 Ndiyeno gulu la mafuko atatu la ana a Efuraimu linanyamuka potengera magulu awo.* Mtsogoleri wa gululi anali Elisama,+ mwana wa Amihudi.