14 Ngati pali mlendo amene akukhala pakati panu, iyenso azikonza nsembe ya Pasika yoti apereke kwa Yehova.+ Aziikonza motsatira malamulo onse a Pasika ndiponso kakonzedwe kake ka nthawi zonse.+ Pakhale malamulo ofanana kwa nonsenu, kaya ndi mlendo kapena mbadwa.’”+