Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 12:49
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 49 Lamulo lililonse lizigwira ntchito mofanana kwa mbadwa ndi kwa mlendo wokhala pakati panu.”+

  • Levitiko 24:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Chigamulo chilichonse chizigwira ntchito mofanana kwa mlendo wokhala pakati panu ndi kwa nzika,+ chifukwa ine ndine Yehova Mulungu wanu.’”

  • Numeri 9:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Ngati pali mlendo amene akukhala pakati panu, iyenso azikonza nsembe ya Pasika yoti apereke kwa Yehova.+ Aziikonza motsatira malamulo onse a Pasika ndiponso kakonzedwe kake ka nthawi zonse.+ Pakhale malamulo ofanana kwa nonsenu, kaya ndi mlendo kapena mbadwa.’”+

  • Numeri 15:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Inu amene ndinu mpingo wa Isiraeli komanso mlendo amene akukhala pakati panu, mukhale ndi malamulo ofanana. Muzitsatira malamulo amenewa mʼmibadwo yanu yonse mpaka kalekale, mlendo komanso inuyo nʼchimodzimodzi pamaso pa Yehova.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena