Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 32:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Choncho iye anati, ‘Ndiwabisira nkhope yanga,+

      Ndione kuti ziwathera bwanji.

      Chifukwa iwo ndi mʼbadwo wokonda zoipa,+

      Ana osakhulupirika.+

  • Salimo 104:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Mukabisa nkhope yanu, zimasokonezeka.

      Mukachotsa mzimu wawo,* zimafa ndipo zimabwerera kufumbi.+

  • Ezekieli 39:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Anthu a mitundu ina adzadziwa kuti a nyumba ya Isiraeli anatengedwa kupita ku ukapolo chifukwa cha zolakwa zawo, popeza anandichitira zinthu mosakhulupirika.+ Choncho ine ndinawabisira nkhope yanga+ nʼkuwapereka kwa adani awo+ ndipo onse anaphedwa ndi lupanga.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena