Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 22:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 ndipo Amowabu anachita mantha kwambiri ndi anthuwo chifukwa anali ambiri. Iwo anagwidwa mantha aakulu chifukwa cha Aisiraeliwo.+

  • Deuteronomo 11:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Palibe munthu amene adzalimbane nanu.+ Yehova Mulungu wanu adzachititsa dziko lonse limene mudzayendemo kugwidwa ndi mantha aakulu ndipo adzakuopani,+ mogwirizana ndi zimene anakulonjezani.

  • Yoswa 5:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Mafumu onse a Aamori+ amene anali kutsidya la kumadzulo kwa mtsinje wa Yorodano, ndi mafumu onse a Akanani+ amene anali mʼmbali mwa nyanja, anamva kuti Yehova anaphwetsa madzi a mtsinje wa Yorodano mpaka Aisiraeli onse atawoloka. Atangomva zimenezo, anachita mantha kwambiri,*+ moti analibenso mphamvu chifukwa choopa Aisiraeli.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena