Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 32:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Choncho Mose anapereka malo kwa ana a Gadi, ana a Rubeni+ komanso hafu ya fuko la Manase+ mwana wa Yosefe. Anawapatsa malo a ufumu wa Sihoni+ mfumu ya Aamori, malo a ufumu wa Ogi+ mfumu ya Basana ndi dera lonse la mizinda komanso midzi yozungulira.

  • Salimo 135:10-12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Anawononga mitundu yambiri+

      Ndipo anapha mafumu amphamvu+

      11 Anapha Sihoni mfumu ya Aamori,+

      Ogi mfumu ya Basana+

      Komanso anawononga maufumu onse a ku Kanani.

      12 Dziko lawo analipereka kuti likhale cholowa,

      Cholowa cha anthu ake Aisiraeli.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena