Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yoswa 10:36, 37
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 36 Kenako Yoswa ndi Aisiraeli onse anachoka ku Egiloni nʼkupita kukamenyana ndi anthu amumzinda wa Heburoni.+ 37 Analanda mzindawo ndipo anapha ndi lupanga mfumu yake, anthu ake onse komanso anthu amʼmidzi yake yonse. Anaonetsetsa kuti pasakhale wopulumuka. Choncho anawononga mzindawo ndi aliyense amene anali mmenemo ngati mmene anachitira ku Egiloni.

  • Yoswa 15:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Kalebe+ mwana wa Yefune anamʼpatsa gawo lake pakati pa ana a Yuda pomvera lamulo la Yehova kwa Yoswa. Anamʼpatsa Kiriyati-ariba, kutanthauza Heburoni. (Ariba anali bambo wa Anaki.)+

  • Yoswa 21:11, 12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Anawapatsa Kiriyati-ariba,+ kutanthauza Heburoni.+ (Ariba anali bambo wa Anaki.) Mzindawu pamodzi ndi malo ouzungulira odyetserako ziweto unali mʼdera lamapiri la Yuda. 12 Koma malo ena onse amumzindawo komanso midzi yake, anawapereka kwa Kalebe mwana wa Yefune kuti akhale ake.+

  • 1 Mbiri 6:55, 56
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 55 Anapatsidwa mzinda wa Heburoni+ mʼdziko la Yuda ndi malo odyetserako ziweto ozungulira mzindawo. 56 Koma malo ena ozungulira mzindawo ndi midzi yake, anawapereka kwa Kalebe+ mwana wa Yefune.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena