Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 23:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Ndikukutumizirani mngelo patsogolo panu+ kuti azikutetezani mʼnjira komanso kukakulowetsani mʼdziko limene ndakukonzerani.+

  • Ekisodo 23:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Chifukwa mngelo wanga adzakutsogolerani nʼkukulowetsani mʼdziko la Aamori, Ahiti, Aperezi, Akanani, Ahivi ndi Ayebusi ndipo ine ndidzawawononga.+

  • Yoswa 5:13, 14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Yoswa ali pafupi ndi Yeriko, anakweza maso ake ndipo anaona mwamuna wina+ ataima patsogolo pake, atanyamula lupanga mʼmanja.+ Yoswa anamuyandikira nʼkumufunsa kuti: “Kodi uli kumbali yathu kapena kumbali ya adani athu?” 14 Munthuyo anayankha kuti: “Ayi, ndabwera chifukwa ndine kalonga* wa gulu lankhondo la Yehova.”+ Atatero, Yoswa anagwada nʼkuwerama mpaka nkhope yake pansi, ndipo anamuuza kuti: “Lankhulani mbuyanga kwa kapolo wanu.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena