Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 17:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Kenako Yehova anauza Mose kuti: “Lemba zimenezi mʼbuku kuti anthu azidzazikumbukira ndipo umuuze Yoswa kuti, ‘Ndidzafafaniziratu Aamaleki padziko lapansi ndipo sadzakumbukiridwa nʼkomwe.’”+

  • Ekisodo 17:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 ndipo anati: “Yehova adzamenya nkhondo ndi Aamaleki ku mibadwomibadwo+ chifukwa dzanja lawo laukira mpando wachifumu wa Ya.”+

  • 1 Samueli 15:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Kenako Sauli anapha Aamaleki+ kuyambira ku Havila+ mpaka ku Shura,+ pafupi ndi Iguputo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena