Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 6:21-7:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Kenako anatumiza uthenga kwa anthu a ku Kiriyati-yearimu+ wakuti: “Afilisiti abweza Likasa la Yehova, bwerani mudzalitenge.”+

      7 Choncho amuna a ku Kiriyati-yearimu anabweradi nʼkutenga Likasa la Yehova ndipo anakaliika mʼnyumba ya Abinadabu+ imene inali paphiri. Ndiyeno anasankha* Eliezara mwana wake kuti azilondera Likasa la Yehova.

  • 2 Samueli 6:1, 2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Davide anasonkhanitsanso asilikali amphamvu mu Isiraeli, okwana 30,000. 2 Ndiyeno Davide ndi anthu onse amene anali naye ananyamuka nʼkupita ku Baale-yuda kuti akatenge Likasa la Mulungu woona.+ Pa likasa limeneli anthu amaitanirapo dzina la Yehova wa magulu ankhondo akumwamba,+ amene amakhala pamwamba* pa akerubi.+

  • 1 Mbiri 15:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Ndiyeno Davide anasonkhanitsa Aisiraeli onse ku Yerusalemu kuti akanyamule Likasa la Yehova, kupita nalo kumalo amene iye anakonza kuti akaliike.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena