Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 23:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Yosiya anachotsanso akachisi onse a mʼmalo okwezeka amene anali mʼmizinda ya ku Samariya,+ omwe mafumu a Isiraeli anamanga kuti akwiyitse Mulungu. Zimene anachita ndi akachisiwa zinali zofanana ndi zimene anachita ku Beteli.+

  • 2 Mbiri 30:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Hezekiya anatumiza uthenga kwa Aisiraeli+ ndi Ayuda onse ndipo analembera makalata anthu a ku Efuraimu ndi ku Manase+ kuti abwere kunyumba ya Yehova ku Yerusalemu kudzachitira Pasika Yehova Mulungu wa Isiraeli.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena