-
2 Mbiri 34:24, 25Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
24 “Yehova wanena kuti, ‘Ndibweretsa tsoka pamalo ano ndiponso kwa anthu ake,+ pokwaniritsa matemberero onse amene analembedwa mʼbuku+ limene anawerenga pamaso pa mfumu ya Yuda, 25 chifukwa chakuti andisiya+ nʼkumakapereka nsembe zautsi kwa milungu ina kuti andikwiyitse+ ndi ntchito zonse za manja awo, ndibweretsa mkwiyo wanga pamalo ano ndipo suzimitsidwa.’”+
-