Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Nehemiya 2:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Kenako ndinawauza kuti: “Inu mukuona vuto lalikulu limene tili nalo. Yerusalemu ndi bwinja ndipo mageti ake anatenthedwa ndi moto. Tiyeni timangenso mpanda wa Yerusalemu kuti anthu asiye kutinyoza.”

  • Nehemiya 6:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Choncho ntchito yomanga mpanda inatha pa tsiku la 25 la mwezi wa Eluli* ndipo inatenga masiku 52.

  • Danieli 9:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Uyenera kudziwa ndi kuzindikira kuti kuchokera pamene lamulo lakuti Yerusalemu akonzedwe ndi kumangidwanso+ lidzaperekedwe kukafika pamene Mesiya*+ Mtsogoleri+ adzaonekere, padzadutsa milungu 7 komanso milungu 62.+ Yerusalemu adzakonzedwa ndi kumangidwanso ndipo adzakhala ndi bwalo ndi ngalande yachitetezo. Koma zimenezi zidzachitika pa nthawi ya mavuto.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena