Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 8:13, 14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Zimenezi ndi zimene zidzachitikire* anthu onse amene aiwala Mulungu,

      Chifukwa chiyembekezo cha anthu oipa* chidzatha,

      14 Anthu amene amadalira zinthu zosathandiza,

      Amene amadalira zinthu zosalimba ngati ulusi wa kangaude.*

  • Yobu 18:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Inde, kuwala kwa woipa kudzazimitsidwa,

      Ndipo malawi a moto wake sadzawala.+

  • Yobu 18:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Iye adzachotsedwa mʼmalo otetezeka amutenti yake,+

      Ndipo adzamupititsa kwa mfumu ya zinthu zoopsa.*

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena