Yobu 30:30 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 30 Khungu langa lada ndipo likusuwa.+Mafupa anga akuwotcha chifukwa cha kutentha.* Salimo 102:5 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 5 Chifukwa chakuti ndikubuula mokweza mawu,+Ndangotsala mafupa okhaokha.+