Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 40:13-17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Mukhale wofunitsitsa kundipulumutsa, inu Yehova.+

      Ndithandizeni mofulumira, inu Yehova.+

      14 Onse amene akufuna kuchotsa moyo wanga

      Achititsidwe manyazi komanso anyozeke.

      Amene akusangalala ndi tsoka langa

      Abwerere mwamanyazi.

      15 Onse amene akunena kuti: “Eyaa! Eyaa!”

      Achite mantha kwambiri chifukwa cha zinthu zochititsa manyazi zimene ziwachitikire.

      16 Koma amene akufunafuna inu,+

      Akondwere ndi kusangalala chifukwa choti akudziwani.+

      Amene amasangalala ndi njira imene mumapulumutsira anthu, nthawi zonse azinena kuti:

      “Yehova alemekezeke.”+

      17 Koma ine ndine munthu wovutika komanso wosauka.

      Yehova aone zimene zikundichitikira.

      Inu ndi amene mumandithandiza komanso kundipulumutsa.+

      Inu Mulungu wanga, musachedwe.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena