Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 17:8, 9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Nditetezeni ngati mwana wa diso lanu,+

      Ndibiseni mumthunzi wa mapiko anu.+

       9 Nditetezeni kwa anthu oipa amene akundiukira,

      Kwa adani* ochokera kufumbi amene andizungulira.+

  • Salimo 59:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 59 Inu Mulungu wanga, ndipulumutseni kwa adani anga.+

      Nditetezeni kwa anthu amene akundiukira.+

  • Salimo 140:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Inu Yehova, nditetezeni kuti manja a munthu woipa asandikhudze.+

      Nditetezeni kwa anthu amene amachita zachiwawa.

      Amene amakonza chiwembu kuti andivulaze.

  • Mateyu 6:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Tithandizeni kuti tisagonje tikamayesedwa,*+ koma mutiteteze kwa woipayo.’+

Mabuku a Chichewa (1974-2026)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena