Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 7:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Inu mukudziwa bwino kuti Yehova Mulungu wanu ndi Mulungu woona, Mulungu wokhulupirika, amene amasunga pangano lake ndiponso amasonyeza chikondi chokhulupirika kwa anthu amene amamukonda ndi kusunga malamulo ake ku mibadwo 1,000.+

  • Luka 1:72, 73
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 72 Adzakwaniritsa zimene analonjeza makolo athu akale ndipo adzawasonyeza chifundo. Iye adzakumbukira pangano lake loyera,+ 73 lumbiro limene analumbira kwa kholo lathu Abulahamu,+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena