Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 22:15-18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Ndiyeno mngelo wa Yehova anaitana Abulahamu kachiwiri kuchokera kumwamba, 16 nʼkumuuza kuti: “Yehova wanena kuti, ‘Ndikulumbira pali dzina langa,+ kuti chifukwa cha zimene wachitazi, posakana kupereka mwana wako mmodzi yekhayo,+ 17 ndidzakudalitsa ndithu. Ndiponso ndidzachulukitsadi mbadwa* zako ngati nyenyezi zakumwamba komanso ngati mchenga wamʼmbali mwa nyanja.+ Ndipo mbadwa yako idzalanda mzinda* wa adani ake.+ 18 Kudzera mwa mbadwa* yako,+ mitundu yonse yapadziko lapansi idzapeza madalitso chifukwa chakuti wamvera mawu anga.’”+

  • Salimo 105:8, 9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Amakumbukira pangano lake mpaka kalekale,+

      Lonjezo limene anapereka* ku mibadwo 1,000.+

       9 Wakumbukira pangano limene anapangana ndi Abulahamu,+

      Komanso lumbiro limene analumbira kwa Isaki,+

  • Mika 7:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Yakobo mudzamusonyeza kukhulupirika.

      Abulahamu mudzamusonyeza chikondi chokhulupirika,

      Ngati mmene munalumbirira kwa makolo athu kalekale.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena