Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 37:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Pamene amalonda a Chimidiyani+ aja ankadutsa, abale a Yosefe anamutulutsa mʼchitsimemo nʼkumugulitsa kwa Aisimaeliwo. Anamugulitsa ndalama zasiliva 20,+ ndipo amalondawo anapita naye ku Iguputo.

  • Genesis 37:36
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 36 Amidiyani aja anakamugulitsa Yosefe ku Iguputo kwa Potifara. Potifara anali nduna yapanyumba ya Farao,+ ndiponso anali mkulu wa asilikali olondera mfumu.+

  • Genesis 45:4, 5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Ndiyeno Yosefe anauza abale akewo kuti: “Sunthirani pafupi ndi ine.” Ndipo anasunthiradi pafupi ndi iye.

      Kenako Yosefe anati: “Ndine mʼbale wanu uja Yosefe, amene munamugulitsa ku Iguputo.+ 5 Koma musadzimvere chisoni kapena kuimbana mlandu kuti munandigulitsa kuno, chifukwa Mulungu ndi amene ananditumiza kuno kuti tikhalebe ndi moyo.+

  • Genesis 50:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Ngakhale kuti munali ndi cholinga chondichitira zoipa,+ Mulungu anali ndi cholinga chabwino, kuti apulumutse miyoyo ya anthu ambiri ngati mmene akuchitira panomu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena