Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 1:1, 2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 1 Wosangalala ndi munthu amene sayenda motsatira malangizo a anthu oipa,

      Saima mʼnjira ya anthu ochimwa,+

      Ndipo sakhala pansi pamodzi ndi anthu onyoza.+

       2 Koma amakonda kwambiri chilamulo cha Yehova,+

      Ndipo amawerenga ndi kuganizira mozama* chilamulocho masana ndi usiku.+

  • Salimo 40:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Ndimasangalala* kuchita zimene mumafuna, inu Mulungu wanga,+

      Ndipo chilamulo chanu chili mumtima mwanga.+

Mabuku a Chichewa (1974-2026)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena