Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 9:13, 14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Ndikomereni mtima inu Yehova. Inu amene mukundichotsa pakhomo la imfa,+

      Onani mmene anthu amene akudana nane akundizunzira,

      14 Kuti ndilengeze ntchito zanu zotamandika pamageti a mwana wamkazi wa Ziyoni,*+

      Komanso kuti ndisangalale chifukwa mwandipulumutsa.+

  • Yesaya 38:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Munthu wamoyo, amene akupuma, ndi amene angakutamandeni,

      Ngati mmene ineyo ndikuchitira lero.

      Bambo akhoza kuphunzitsa ana ake za kukhulupirika kwanu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena