Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 8:12, 13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Pa nthawiyo Solomo ananena kuti: “Yehova anati adzakhala mumdima wandiweyani.+ 13 Ine ndakwanitsa kukumangirani nyumba yapamwamba yomwe ndi malo okhazikika oti muzikhalamo mpaka kalekale.”+

  • Salimo 48:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Phiri la Ziyoni limene lili mʼdera lakutali lakumpoto,

      Ndi lokongola chifukwa lili pamalo okwezeka komanso anthu padziko lonse lapansi akusangalala nalo,+

      Ndipo ndi mzinda wa Mfumu Yaikulu.+

  • Salimo 132:13, 14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Chifukwa Yehova wasankha Ziyoni.+

      Akufunitsitsa kuti akhale malo ake okhalamo. Iye akuti:+

      14 “Awa ndi malo anga okhalamo mpaka kalekale.

      Ndidzakhala mmenemu,+ chifukwa zimenezi ndi zimene ndikulakalaka.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena