Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 2:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Iye adzawauza kuti: “Inetu ndasankha mfumu yanga+

      Ndipo ikulamulira ku Ziyoni,+ phiri langa lopatulika.”

  • Salimo 72:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Iye adzakhala ndi anthu omugonjera* kuchokera kunyanja kukafika kunyanja,

      Komanso kuchokera ku Mtsinje* kukafika kumalekezero a dziko lapansi.+

  • Yesaya 9:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Chifukwa kwa ife kwabadwa mwana,+

      Ife tapatsidwa mwana wamwamuna,

      Ndipo ulamuliro* udzakhala paphewa pake.+

      Iye adzapatsidwa dzina lakuti Mlangizi Wodabwitsa,+ Mulungu Wamphamvu,+ Atate Wamuyaya, Kalonga Wamtendere.

  • Chivumbulutso 11:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Mngelo wa 7 analiza lipenga lake.+ Ndiyeno kumwamba kunamveka mawu osiyanasiyana akunena mokweza kuti: “Ufumu wa dziko wakhala Ufumu wa Ambuye wathu+ ndi wa Khristu wake+ ndipo iye adzalamulira monga mfumu mpaka kalekale.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena