Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 32:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Pamene ndinakhala chete osaulula machimo anga, mafupa anga anafooka, chifukwa ndinkavutika mumtima mwanga tsiku lonse.+

  • Salimo 102:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Chifukwa masiku a moyo wanga akuzimiririka ngati utsi,

      Ndipo mafupa anga akutentha kwambiri ngati ngʼanjo.+

  • Salimo 102:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Chifukwa chakuti ndikubuula mokweza mawu,+

      Ndangotsala mafupa okhaokha.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena