Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 141:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Wolungama akandimenya ndiye kuti wandisonyeza chikondi chokhulupirika.+

      Akandidzudzula zingakhale ngati wandidzoza mafuta pamutu,+

      Mafuta amene mutu wanga sungawakane.+

      Ndidzapemphererabe anthu olungama ngakhale pamene masoka awagwera.

  • Miyambo 27:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Mabala ovulazidwa ndi mnzako amakhala okhulupirika,+

      Koma makisi a munthu* amene amadana nawe amakhala ambiri.*

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena