Zekariya 13:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 “Iwe lupanga, nyamuka ubaye mʼbusa wanga.+Ubaye munthu yemwe ndi mnzanga,” watero Yehova wa magulu ankhondo akumwamba. “Ipha mʼbusa+ ndipo nkhosa zake zibalalike.+Ine ndidzalanga nkhosa zonyozeka.” Yohane 11:49, 50 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 49 Koma mmodzi wa iwo, Kayafa,+ amene anali mkulu wa ansembe chaka chimenecho, anati: “Palibe chimene mukudziwa inu 50 ndipo simukuona kuti nʼzothandiza kwa inu kuti munthu mmodzi afere anthu onse mʼmalo moti mtundu wonse uwonongeke.” Aroma 5:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Pamene tinalibe mtengo wogwira,*+ Khristu anafera anthu osalambira Mulungu pa nthawi imene anakonzeratu. Aheberi 9:26 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 26 Zikanatero, akanavutika mobwerezabwereza kuyambira pamene dziko linakhazikitsidwa. Koma tsopano iye waonekera kamodzi kokha pamapeto a nthawi* ino kuti achotse uchimo kudzera mu nsembe yake.+
7 “Iwe lupanga, nyamuka ubaye mʼbusa wanga.+Ubaye munthu yemwe ndi mnzanga,” watero Yehova wa magulu ankhondo akumwamba. “Ipha mʼbusa+ ndipo nkhosa zake zibalalike.+Ine ndidzalanga nkhosa zonyozeka.”
49 Koma mmodzi wa iwo, Kayafa,+ amene anali mkulu wa ansembe chaka chimenecho, anati: “Palibe chimene mukudziwa inu 50 ndipo simukuona kuti nʼzothandiza kwa inu kuti munthu mmodzi afere anthu onse mʼmalo moti mtundu wonse uwonongeke.”
6 Pamene tinalibe mtengo wogwira,*+ Khristu anafera anthu osalambira Mulungu pa nthawi imene anakonzeratu.
26 Zikanatero, akanavutika mobwerezabwereza kuyambira pamene dziko linakhazikitsidwa. Koma tsopano iye waonekera kamodzi kokha pamapeto a nthawi* ino kuti achotse uchimo kudzera mu nsembe yake.+