Salimo 42:2 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 2 Mofanana ndi munthu amene akulakalaka madzi, ndikulakalaka* Mulungu, Mulungu wamoyo.+ Ndidzapita liti kukaonekera pamaso pa Mulungu?*+ Salimo 63:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 63 Inu Mulungu, ndinu Mulungu wanga, ine ndikukufunafunani.+ Ine ndikulakalaka inu.*+ Ndalefuka* chifukwa cholakalaka inuMʼdziko louma komanso lopanda madzi, kumene sikumera chilichonse.+ Amosi 8:11 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, wanena kuti, ‘Taonani, masiku akubweraPamene ndidzatumiza njala mʼdziko.Osati njala ya chakudya kapena ludzu lofuna madzi,Koma njala yofuna kumva mawu a Yehova.+ Mateyu 5:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Osangalala ndi anthu amene akumva njala ndi ludzu+ la chilungamo chifukwa adzakhuta.+
2 Mofanana ndi munthu amene akulakalaka madzi, ndikulakalaka* Mulungu, Mulungu wamoyo.+ Ndidzapita liti kukaonekera pamaso pa Mulungu?*+
63 Inu Mulungu, ndinu Mulungu wanga, ine ndikukufunafunani.+ Ine ndikulakalaka inu.*+ Ndalefuka* chifukwa cholakalaka inuMʼdziko louma komanso lopanda madzi, kumene sikumera chilichonse.+
11 Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, wanena kuti, ‘Taonani, masiku akubweraPamene ndidzatumiza njala mʼdziko.Osati njala ya chakudya kapena ludzu lofuna madzi,Koma njala yofuna kumva mawu a Yehova.+