Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 21:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Tiyeni tiwalase.

      Hesiboni adzawonongedwa mpaka ku Diboni.+

      Tiyeni timusandutse bwinja mpaka ku Nofa,

      Moto udzafalikira mpaka ku Medeba.”+

  • Yoswa 13:15-17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Kenako Mose anagawira cholowa fuko la Rubeni motsatira mabanja awo. 16 Dera lawo linayambira ku Aroweli, mzinda umene uli mʼmbali mwa chigwa cha Arinoni, ndiponso mzinda umene uli pakatikati pa chigwacho komanso malo onse okwera a Medeba. 17 Linafikanso ku Hesiboni ndi midzi yake yonse+ imene inali mʼmalo okwera, ku Diboni, ku Bamoti-baala komanso ku Beti-baala-meoni.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena