Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 12:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Alangizi okhulupirika amawasowetsa chonena,

      Ndipo amachotsa kuzindikira kwa amuna achikulire,*

  • Yobu 12:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Amachotsa nzeru za atsogoleri* a anthuwo,

      Ndipo amawachititsa kuti azingoyendayenda mʼchipululu mmene mulibe njira.+

  • Yesaya 19:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Anthu a mu Iguputo adzadabwa kwambiri

      Ndipo ine ndidzasokoneza mapulani awo.+

      Iwo adzafunsira kwa milungu yopanda pake,

      Kwa anthu amatsenga, kwa olankhula ndi mizimu ndiponso kwa olosera zamʼtsogolo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena