Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 85:2, 3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Munakhululukira anthu anu zolakwa zawo.

      Munawakhululukira* machimo awo onse.+ (Selah)

       3 Munabweza mkwiyo wanu wonse,

      Ndipo simunasonyeze mkwiyo wanu waukulu.+

  • Yesaya 12:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Pa tsiku limenelo ndithu udzanena kuti:

      “Ndikukuthokozani, inu Yehova

      Chifukwa ngakhale munandikwiyira,

      Mkwiyo wanu unachepa pangʼonopangʼono ndipo munanditonthoza.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena