Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Nehemiya 13:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Ndiyeno ndinauza Alevi kuti azidziyeretsa nthawi zonse komanso azibwera kudzalondera mageti a mzinda kuti tsiku la Sabata likhale loyera.+ Inu Mulungu wanga, mundikumbukirenso pa zimenezi ndipo mundichitire chifundo mogwirizana ndi kuchuluka kwa chikondi chanu chokhulupirika.+

  • Salimo 20:1-3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Yehova akuyankheni pa tsiku la mavuto.

      Dzina la Mulungu wa Yakobo likutetezeni.+

       2 Akutumizireni thandizo kuchokera kumalo ake opatulika+

      Ndipo akuthandizeni ali ku Ziyoni.+

       3 Akumbukire nsembe zanu zonse zimene munapereka monga mphatso.

      Alandire mosangalala* nsembe zanu zopsereza. (Selah)

  • Aheberi 6:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Chifukwa Mulungu si wosalungama kuti angaiwale ntchito yanu ndiponso chikondi chimene munachisonyeza pa dzina lake,+ potumikira oyera ndipo mukupitiriza kuwatumikira.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena