Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 30:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Inu Yehova, mwanditulutsa mʼManda,*+

      Mwandisunga ndi moyo, mwanditeteza kuti ndisatsikire mʼdzenje.*+

  • Salimo 86:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Chifukwa chikondi chanu chokhulupirika chimene mumandisonyeza ndi chachikulu

      Ndipo mwapulumutsa moyo wanga ku dzenje la Manda.*+

  • Yona 2:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Ndinamira mpaka mʼmunsi mwenimweni mwa mapiri.

      Zotsekera za dziko lapansi zinayamba kunditsekereza kuti ndikhale komweko mpaka kalekale.

      Koma inu Yehova Mulungu wanga, munanditulutsa mʼdzenje ndili wamoyo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena