Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mbiri 34:20, 21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Kenako mfumuyo inalamula Hilikiya, Ahikamu+ mwana wa Safani, Abidoni mwana wa Mika, Safani mlembi ndi Asaya mtumiki wa mfumu, kuti: 21 “Pitani mukafunsire kwa Yehova mʼmalo mwa ineyo ndiponso mʼmalo mwa anthu amene atsala mu Isiraeli ndi mu Yuda. Mukafunse zokhudza mawu amʼbuku limene lapezekali, chifukwa mkwiyo umene Yehova adzatisonyeze ndi waukulu, popeza makolo athu sanasunge mawu a Yehova moti sanatsatire zonse zimene zinalembedwa mʼbukuli.”+

  • Yeremiya 26:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Koma Ahikamu,+ mwana wa Safani+ anateteza Yeremiya, nʼchifukwa chake sanaperekedwe kwa anthu kuti amuphe.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena