Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yeremiya 36:22-24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Pa nthawiyi nʼkuti mfumu ili mʼnyumba imene inkakhala mʼnyengo yozizira ndipo inkawotha moto wamʼmbaula. Umenewu unali mwezi wa 9.* 23 Yehudi akawerenga zigawo zitatu kapena 4 za mpukutuwo, mfumu inkadula mpukutuwo ndi mpeni wa mlembi nʼkuponya chidutswacho pamoto umene unali mʼmbaula uja. Inachita izi mpaka mpukutu wonsewo unathera pamotopo. 24 Iwo sanachite mantha ndipo mfumu ndi atumiki ake onse amene ankamvetsera mawuwa sanangʼambe zovala zawo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena