Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 10:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Ana a Hamu anali Kusi, Miziraimu,+ Puti+ ndi Kanani.+

  • Genesis 10:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Miziraimu anabereka Ludimu,+ Anamimu, Lehabimu, Nafituhimu,+

  • Ezekieli 30:4, 5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Lupanga lidzabwera kudzaukira Iguputo, ndipo anthu a ku Itiyopiya adzachita mantha kwambiri anthu akadzaphedwa ku Iguputo.

      Chuma cha Iguputo chidzalandidwa ndipo maziko ake adzagwetsedwa.+

       5 Itiyopiya,+ Puti,+ Ludi, anthu onse ochokera mʼmitundu yosiyanasiyana,

      Kubi limodzi ndi anthu amʼdziko lapangano,*

      Onsewa adzaphedwa ndi lupanga.”’

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena