Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 44:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Ndine amene ndikuuza madzi akuya kuti, ‘Iphwa

      Ndipo mitsinje yako yonse ndidzaiumitsa.’+

  • Yeremiya 51:36, 37
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 36 Choncho Yehova wanena kuti:

      “Ine ndikuteteza pa mlandu wako,+

      Ndipo ndidzakubwezerera adani ako.+

      Ndidzaphwetsa nyanja yake ndi zitsime zake.+

      37 Babulo adzakhala milu yamiyala,+

      Malo obisalamo mimbulu,+

      Chinthu chochititsa mantha komanso chimene anthu azidzachiimbira mluzu

      Ndipo simudzapezeka munthu wokhalamo.+

  • Chivumbulutso 16:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Mngelo wa 6 anathira mbale yake pamtsinje waukulu wa Firate+ ndipo madzi ake anauma,+ kuti njira ya mafumu+ ochokera kotulukira dzuwa* ikonzedwe.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena