Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 28:25, 26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Yehova adzachititsa kuti adani anu akugonjetseni.+ Popita kukawaukira mudzadutsa njira imodzi, koma pothawa mudzadutsa njira zosiyanasiyana 7. Mafumu onse a dziko lapansi adzachita mantha akadzaona zinthu zoipa zimene zakuchitikirani.+ 26 Mitembo yanu idzakhala chakudya cha mbalame zonse zouluka mumlengalenga ndi zilombo zoyenda panthaka, ndipo sipadzapezeka woziopseza.+

  • Salimo 79:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Apereka mitembo ya atumiki anu kwa mbalame kuti chikhale chakudya chawo

      Ndipo matupi a anthu anu okhulupirika awapereka kwa zilombo zakutchire.+

  • Yeremiya 7:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Mitembo ya anthu awa idzakhala chakudya cha mbalame zouluka mumlengalenga ndi cha zilombo ndipo sipadzakhala woziopseza.+

  • Yeremiya 16:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 ‘Iwo adzafa ndi matenda oopsa+ koma palibe amene adzalire maliro awo kapena kuwaika mʼmanda. Iwo adzakhala ngati manyowa panthaka.+ Adzafa ndi lupanga ndiponso njala.+ Mitembo yawo idzakhala chakudya cha mbalame zamumlengalenga ndi zilombo zakutchire.’

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena