Yeremiya 50:19 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 19 Isiraeli ndidzamubwezeretsa kumalo ake odyerako msipu+ moti adzadya msipu paphiri la Karimeli ndi ku Basana.+ Ndipo iye adzakhutira mʼmapiri a Efuraimu+ ndi Giliyadi.’”+ Ezekieli 34:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 Nkhosazo ndidzazidyetsera mʼmalo a msipu wabwino ndipo malo amene zizidzadya msipu adzakhala kumapiri ataliatali a ku Isiraeli.+ Kumeneko zizidzagona pansi mʼmalo abwino kwambiri odyetserako ziweto+ ndipo zizidzadya msipu wabwino kwambiri mʼmapiri a ku Isiraeli. Mika 2:12 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 12 Ndithu ndidzasonkhanitsa mbadwa zonse za Yakobo.Ndidzasonkhanitsa Aisiraeli otsala.+ Ndidzawabweretsa pamalo amodzi ngati gulu la nkhosa mʼkhola,Komanso ngati gulu la ziweto pamalo amsipu.+Kumeneko kudzakhala phokoso la anthu.’+
19 Isiraeli ndidzamubwezeretsa kumalo ake odyerako msipu+ moti adzadya msipu paphiri la Karimeli ndi ku Basana.+ Ndipo iye adzakhutira mʼmapiri a Efuraimu+ ndi Giliyadi.’”+
14 Nkhosazo ndidzazidyetsera mʼmalo a msipu wabwino ndipo malo amene zizidzadya msipu adzakhala kumapiri ataliatali a ku Isiraeli.+ Kumeneko zizidzagona pansi mʼmalo abwino kwambiri odyetserako ziweto+ ndipo zizidzadya msipu wabwino kwambiri mʼmapiri a ku Isiraeli.
12 Ndithu ndidzasonkhanitsa mbadwa zonse za Yakobo.Ndidzasonkhanitsa Aisiraeli otsala.+ Ndidzawabweretsa pamalo amodzi ngati gulu la nkhosa mʼkhola,Komanso ngati gulu la ziweto pamalo amsipu.+Kumeneko kudzakhala phokoso la anthu.’+