Yesaya 11:16 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 16 Padzakhala msewu waukulu+ wochokera kudziko la Asuri woti mudzadutse anthu ake amene adzatsale,+Ngati mmene zinalili kwa Aisiraeli pamene ankatuluka mʼdziko la Iguputo. Yesaya 65:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Sharoni+ adzakhala malo odyetserako nkhosaNdipo chigwa cha Akori+ chidzakhala malo opumulirapo ngʼombe,Anthu anga amene akundifunafuna ndidzawachitira zimenezi. Yeremiya 23:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 “Kenako ndidzasonkhanitsa pamodzi nkhosa zanga zotsala kuchokera mʼmayiko onse kumene ndinazibalalitsira+ ndipo ndidzazibwezeretsa kumalo awo kumene zimadyera.+ Nkhosazo zidzaberekana ndi kuchuluka.+ Yeremiya 33:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Anthu a mu Yuda ndi a mu Isiraeli amene anatengedwa kupita kudziko lina ndidzawabwezeretsa+ ndipo adzakhalanso ngati mmene analili poyamba.+ Ezekieli 34:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 Nkhosazo ndidzazidyetsera mʼmalo a msipu wabwino ndipo malo amene zizidzadya msipu adzakhala kumapiri ataliatali a ku Isiraeli.+ Kumeneko zizidzagona pansi mʼmalo abwino kwambiri odyetserako ziweto+ ndipo zizidzadya msipu wabwino kwambiri mʼmapiri a ku Isiraeli. Mika 2:12 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 12 Ndithu ndidzasonkhanitsa mbadwa zonse za Yakobo.Ndidzasonkhanitsa Aisiraeli otsala.+ Ndidzawabweretsa pamalo amodzi ngati gulu la nkhosa mʼkhola,Komanso ngati gulu la ziweto pamalo amsipu.+Kumeneko kudzakhala phokoso la anthu.’+
16 Padzakhala msewu waukulu+ wochokera kudziko la Asuri woti mudzadutse anthu ake amene adzatsale,+Ngati mmene zinalili kwa Aisiraeli pamene ankatuluka mʼdziko la Iguputo.
10 Sharoni+ adzakhala malo odyetserako nkhosaNdipo chigwa cha Akori+ chidzakhala malo opumulirapo ngʼombe,Anthu anga amene akundifunafuna ndidzawachitira zimenezi.
3 “Kenako ndidzasonkhanitsa pamodzi nkhosa zanga zotsala kuchokera mʼmayiko onse kumene ndinazibalalitsira+ ndipo ndidzazibwezeretsa kumalo awo kumene zimadyera.+ Nkhosazo zidzaberekana ndi kuchuluka.+
7 Anthu a mu Yuda ndi a mu Isiraeli amene anatengedwa kupita kudziko lina ndidzawabwezeretsa+ ndipo adzakhalanso ngati mmene analili poyamba.+
14 Nkhosazo ndidzazidyetsera mʼmalo a msipu wabwino ndipo malo amene zizidzadya msipu adzakhala kumapiri ataliatali a ku Isiraeli.+ Kumeneko zizidzagona pansi mʼmalo abwino kwambiri odyetserako ziweto+ ndipo zizidzadya msipu wabwino kwambiri mʼmapiri a ku Isiraeli.
12 Ndithu ndidzasonkhanitsa mbadwa zonse za Yakobo.Ndidzasonkhanitsa Aisiraeli otsala.+ Ndidzawabweretsa pamalo amodzi ngati gulu la nkhosa mʼkhola,Komanso ngati gulu la ziweto pamalo amsipu.+Kumeneko kudzakhala phokoso la anthu.’+