Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 16:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Pambuyo pake, mngelo wa Yehova anakumana ndi Hagara mʼchipululu ali pakasupe wamadzi. Kasupeyo anali panjira yopita ku Shura.+

  • Genesis 16:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Ndiyeno Hagara anapemphera kwa Yehova* kuti: “Inu ndinu Mulungu amene amaona chilichonse.”+ Ananenanso kuti: “Kodi nanenso pano ndaona amene amatha kundionayo?”

  • Miyambo 15:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Maso a Yehova ali paliponse,

      Amaona anthu oipa ndi abwino omwe.+

  • Amosi 9:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Akadzakumba Manda* kuti abisalemo,

      Ndidzawatulutsa ndi dzanja langa.

      Ndipo akadzakwera kumwamba,

      Ndidzawatsitsira pansi.

  • Aheberi 4:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Palibe cholengedwa chimene Mulungu sangathe kuchiona.+ Chifukwa kwa iye zinthu zonse zili poonekera ndipo amatha kuziona bwinobwino moti ifeyo tidzayankha kwa Mulunguyo pa zochita zathu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena