-
Yesaya 3:1Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
3 Tamverani! Ambuye woona, Yehova wa magulu ankhondo akumwamba,
Akuchotsa mu Yerusalemu ndi mu Yuda zinthu zonse zofunika pa moyo,
Monga mkate ndi madzi.+
-