Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yoweli 2:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 “Lizani lipenga mu Ziyoni.+

      Lengezani mʼphiri langa loyera kuti kukubwera nkhondo.

      Anthu onse okhala mʼdzikoli anjenjemere,

      Chifukwa tsiku la Yehova likubwera+ ndipo lili pafupi.

  • Zefaniya 1:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Tsiku lalikulu la Yehova lili pafupi.+

      Lili pafupi ndipo likubwera mofulumira kwambiri.+

      Mkokomo wa tsiku la Yehova ukubwera ndi zowawa.+

      Pa tsiku limenelo msilikali adzalira.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena