-
Yesaya 3:1Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
3 Tamverani! Ambuye woona, Yehova wa magulu ankhondo akumwamba,
Akuchotsa mu Yerusalemu ndi mu Yuda zinthu zonse zofunika pa moyo,
Monga mkate ndi madzi.+
-
Yeremiya 15:2Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
2 Ndiyeno akakufunsa kuti, ‘Tipite kuti?’ uwayankhe kuti, ‘Yehova wanena kuti:
“Amene akuyenera kufa ndi mliri afe ndi mliri!
Amene akuyenera kufa ndi lupanga afe ndi lupanga!+
Amene akuyenera kufa ndi njala yaikulu afe ndi njala yaikulu!
Amene akuyenera kutengedwa kupita ku ukapolo atengedwe kupita ku ukapolo!”’+
-
-
-