Ekisodo 32:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 32 Mose ali mʼphirimo, anthu anaona kuti akuchedwa kutsika.+ Choncho anthuwo anasonkhana kwa Aroni nʼkumuuza kuti: “Tipangire mulungu woti atitsogolere,+ chifukwa sitikudziwa zimene zachitikira Mose, amene ankatitsogolera pochoka ku Iguputo.” Ekisodo 32:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 Kenako iye analandira golideyo kuchokera kwa anthuwo ndipo pogwiritsa ntchito chosemera, anapanga fano* la mwana wa ngʼombe.+ Zitatero iwo anayamba kunena kuti: “Uyu ndi Mulungu wanu, Aisiraeli inu, amene anakutulutsani mʼdziko la Iguputo.”+ Numeri 25:1, 2 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 25 Pa nthawi imene Aisiraeli ankakhala ku Sitimu,+ anayamba kuchita chiwerewere ndi akazi a ku Mowabu.+ 2 Akaziwo anaitana Aisiraeliwo kuti azikapereka nsembe kwa milungu yawo+ ndipo Aisiraeliwo anayamba kudya nsembezo komanso kugwadira milungu ya Amowabu.+ Machitidwe 7:42 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 42 Choncho Mulungu anawasiya kuti atumikire magulu akumwamba+ ngati mmene malemba amanenera mʼbuku la Aneneri. Malembawo amati, ‘Anthu inu a nyumba ya Isiraeli, kodi mʼchipululu muja munkapereka kwa ine nsembe ndi zopereka zina kwa zaka 40?
32 Mose ali mʼphirimo, anthu anaona kuti akuchedwa kutsika.+ Choncho anthuwo anasonkhana kwa Aroni nʼkumuuza kuti: “Tipangire mulungu woti atitsogolere,+ chifukwa sitikudziwa zimene zachitikira Mose, amene ankatitsogolera pochoka ku Iguputo.”
4 Kenako iye analandira golideyo kuchokera kwa anthuwo ndipo pogwiritsa ntchito chosemera, anapanga fano* la mwana wa ngʼombe.+ Zitatero iwo anayamba kunena kuti: “Uyu ndi Mulungu wanu, Aisiraeli inu, amene anakutulutsani mʼdziko la Iguputo.”+
25 Pa nthawi imene Aisiraeli ankakhala ku Sitimu,+ anayamba kuchita chiwerewere ndi akazi a ku Mowabu.+ 2 Akaziwo anaitana Aisiraeliwo kuti azikapereka nsembe kwa milungu yawo+ ndipo Aisiraeliwo anayamba kudya nsembezo komanso kugwadira milungu ya Amowabu.+
42 Choncho Mulungu anawasiya kuti atumikire magulu akumwamba+ ngati mmene malemba amanenera mʼbuku la Aneneri. Malembawo amati, ‘Anthu inu a nyumba ya Isiraeli, kodi mʼchipululu muja munkapereka kwa ine nsembe ndi zopereka zina kwa zaka 40?