Danieli 10:13 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 13 Koma kalonga+ wa ufumu wa Perisiya ananditsekereza kwa masiku 21. Ndiyeno Mikayeli,*+ mmodzi wa akalonga aakulu,* anabwera kudzandithandiza. Pa nthawi imeneyo ndinakhalabe pomwepo pafupi ndi mafumu a Perisiya. Yuda 9 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 9 Koma pamene Mikayeli,+ mkulu wa angelo,+ anasemphana maganizo ndi Mdyerekezi ndipo anakangana naye za mtembo wa Mose,+ sanayese nʼkomwe kumuweruza komanso kumunyoza,+ mʼmalomwake anati: “Yehova* akudzudzule.”+ Chivumbulutso 12:7, 8 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Ndipo kumwamba kunabuka nkhondo: Mikayeli*+ ndi angelo ake anamenyana ndi chinjoka. Chinjokacho ndi angelo ake chinamenya nkhondo, 8 koma sanapambane* ndipo malo awo sanapezekenso kumwamba.
13 Koma kalonga+ wa ufumu wa Perisiya ananditsekereza kwa masiku 21. Ndiyeno Mikayeli,*+ mmodzi wa akalonga aakulu,* anabwera kudzandithandiza. Pa nthawi imeneyo ndinakhalabe pomwepo pafupi ndi mafumu a Perisiya.
9 Koma pamene Mikayeli,+ mkulu wa angelo,+ anasemphana maganizo ndi Mdyerekezi ndipo anakangana naye za mtembo wa Mose,+ sanayese nʼkomwe kumuweruza komanso kumunyoza,+ mʼmalomwake anati: “Yehova* akudzudzule.”+
7 Ndipo kumwamba kunabuka nkhondo: Mikayeli*+ ndi angelo ake anamenyana ndi chinjoka. Chinjokacho ndi angelo ake chinamenya nkhondo, 8 koma sanapambane* ndipo malo awo sanapezekenso kumwamba.