Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 2:7-9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Ndifotokoza zimene Yehova wanena.

      Iye wandiuza kuti: “Iwe ndiwe mwana wanga,+

      Lero, ine ndakhala bambo ako.+

       8 Tandipempha, ndipo ndikupatsa mitundu ya anthu kuti ikhale cholowa chako,

      Ndiponso dziko lonse lapansi kuti likhale lako.+

       9 Mitunduyo udzaiphwanya ndi ndodo yachifumu yachitsulo,+

      Ndipo udzaiswa ngati chiwiya chadothi.”+

  • Salimo 110:5, 6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Yehova adzakhala kudzanja lako lamanja.+

      Iye adzaphwanya mafumu pa tsiku la mkwiyo wake.+

       6 Adzapereka chiweruzo ku* mitundu ya anthu.+

      Adzachititsa kuti mʼdziko mudzaze mitembo ya anthu.+

      Adzaphwanya mtsogoleri* wa dziko lalikulu.*

  • Chivumbulutso 19:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Mʼkamwa mwake munkatuluka lupanga lalitali+ lakuthwa, loti aphere mitundu ya anthu ndipo adzawakusa ndi ndodo yachitsulo.+ Komanso iye ankapondaponda muchopondera mphesa cha mkwiyo waukulu wa Mulungu Wamphamvuyonse.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena