Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yeremiya 50:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Isiraeli ndidzamubwezeretsa kumalo ake odyerako msipu+ moti adzadya msipu paphiri la Karimeli ndi ku Basana.+ Ndipo iye adzakhutira mʼmapiri a Efuraimu+ ndi Giliyadi.’”+

  • Mika 7:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Weta anthu ako ndi ndodo yako, gulu la nkhosa zomwe ndi cholowa chako,+

      Zimene zinkakhala zokhazokha mʼnkhalango komanso pakati pa mitengo ya zipatso.

      Uzilole zikadyere ku Basana ndi ku Giliyadi+ ngati mmene zinkachitira kale.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena