Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 20:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Musachite chigololo.+

  • Deuteronomo 5:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Musachite chigololo.+

  • Luka 18:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Iwe umadziwa malamulo akuti: ‘Musachite chigololo,+ musaphe munthu,*+ musabe,+ musapereke umboni wabodza+ ndiponso lakuti, muzilemekeza bambo anu ndi mayi anu.’”+

  • Aroma 13:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Chifukwa malamulo onena kuti, “usachite chigololo,+ usaphe munthu,+ usabe,+ usasirire mwansanje,”+ ndiponso lamulo lina lililonse limene lilipo, chidule chake chili mʼmawu awa akuti: “Uzikonda mnzako mmene umadzikondera wekha.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena