Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mateyu 26:55, 56
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 55 Mu ola lomwelo Yesu anafunsa gulu la anthulo kuti: “Bwanji mwabwera kudzandigwira mutatenga malupanga ndi zibonga ngati mukudzalimbana ndi wachifwamba? Tsiku ndi tsiku ndinkakhala pansi mʼkachisi nʼkumaphunzitsa,+ koma simunandigwire.+ 56 Koma zonsezi zachitika kuti zimene aneneri analemba zikwaniritsidwe.”*+ Kenako ophunzira ake onse anamuthawa nʼkumusiya yekha.+

  • Luka 22:52, 53
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 52 Ndiyeno Yesu anafunsa ansembe aakulu, oyangʼanira kachisi ndi akulu amene anabwera kudzamugwira kuti: “Bwanji mwabwera ndi malupanga ndi zibonga ngati mukudzalimbana ndi wachifwamba?+ 53 Tsiku ndi tsiku ndinali nanu mʼkachisi+ koma simunandigwire.+ Koma ino tsopano ndi nthawi yanu komanso nthawi ya ulamuliro wamdima.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena